×

Kumbukira za m’bale wa anthu a mtundu wa Aad pamene iye adawachenjeza 46:21 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahqaf ⮕ (46:21) ayat 21 in Chichewa

46:21 Surah Al-Ahqaf ayat 21 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahqaf ayat 21 - الأحقَاف - Page - Juz 26

﴿۞ وَٱذۡكُرۡ أَخَا عَادٍ إِذۡ أَنذَرَ قَوۡمَهُۥ بِٱلۡأَحۡقَافِ وَقَدۡ خَلَتِ ٱلنُّذُرُ مِنۢ بَيۡنِ يَدَيۡهِ وَمِنۡ خَلۡفِهِۦٓ أَلَّا تَعۡبُدُوٓاْ إِلَّا ٱللَّهَ إِنِّيٓ أَخَافُ عَلَيۡكُمۡ عَذَابَ يَوۡمٍ عَظِيمٖ ﴾
[الأحقَاف: 21]

Kumbukira za m’bale wa anthu a mtundu wa Aad pamene iye adawachenjeza anthu ake m’chipululu. Ndithudi kudali Achenjezi ena iye asanabadwe ndi atachoka amene amati, “Musapembedze wina aliyense kupatula Mulungu chifukwa ndiopa chilango chowawa chimene chingadze pa inu patsiku lachiweruzo.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: واذكر أخا عاد إذ أنذر قومه بالأحقاف وقد خلت النذر من بين, باللغة نيانجا

﴿واذكر أخا عاد إذ أنذر قومه بالأحقاف وقد خلت النذر من بين﴾ [الأحقَاف: 21]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo kumbuka za m’bale wa Âdi, (mtumiki Hûd) pamene adachenjeza anthu ake kudziko la milu ya mchenga. Ndithu adaliponso achenjezi iye asadadze ndiponso iye atapita. (Iye adawauza anthu ake): “Musampembedze aliyense koma Allah; ndithu ine ndikukuoperani chilango cha tsiku lalikulu.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek