×

Ndipo iwe umawaona anthu amene ali ndi matenda m’mitima mwawo ali kuwathamangira 5:52 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:52) ayat 52 in Chichewa

5:52 Surah Al-Ma’idah ayat 52 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 52 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿فَتَرَى ٱلَّذِينَ فِي قُلُوبِهِم مَّرَضٞ يُسَٰرِعُونَ فِيهِمۡ يَقُولُونَ نَخۡشَىٰٓ أَن تُصِيبَنَا دَآئِرَةٞۚ فَعَسَى ٱللَّهُ أَن يَأۡتِيَ بِٱلۡفَتۡحِ أَوۡ أَمۡرٖ مِّنۡ عِندِهِۦ فَيُصۡبِحُواْ عَلَىٰ مَآ أَسَرُّواْ فِيٓ أَنفُسِهِمۡ نَٰدِمِينَ ﴾
[المَائدة: 52]

Ndipo iwe umawaona anthu amene ali ndi matenda m’mitima mwawo ali kuwathamangira abwenzi awo nati: “Tili kuopa kuti mwina tsoka likhoza kutigwera ife.” Mwina Mulungu akhoza kubweretsa kupambana kapena lamulo mwachifuniro chake. Ndipo iwo adzadandaula chifukwa cha zimene adasunga ngati chinsinsi mwa iwo okha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فترى الذين في قلوبهم مرض يسارعون فيهم يقولون نخشى أن تصيبنا دائرة, باللغة نيانجا

﴿فترى الذين في قلوبهم مرض يسارعون فيهم يقولون نخشى أن تصيبنا دائرة﴾ [المَائدة: 52]

Khaled Ibrahim Betala
“Uwaona omwe m’mitima mwawo muli matenda (a chinyengo) akuthamangira kwa iwo (Ayuda) uku akuti: “Tikuopa lingatigwere tsoka (ngati Asilamuwa atagwa m’tsoka), koma posachedwapa Allah abweretsa lamulo logonjetsa (midzi), kapena chinthu china chochokera kwa Iye (monga kuwaulula achinyengo zomwe akubisa m’mitima mwawo). Choncho adzasanduka odzinena chifukwa cha zomwe adabisa m’mitima mwawo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek