×

Ndipo anthu okhulupirira adzati; “Kodi awa ndi anthu omwe analumbira molimbika kuti, 5:53 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:53) ayat 53 in Chichewa

5:53 Surah Al-Ma’idah ayat 53 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 53 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿وَيَقُولُ ٱلَّذِينَ ءَامَنُوٓاْ أَهَٰٓؤُلَآءِ ٱلَّذِينَ أَقۡسَمُواْ بِٱللَّهِ جَهۡدَ أَيۡمَٰنِهِمۡ إِنَّهُمۡ لَمَعَكُمۡۚ حَبِطَتۡ أَعۡمَٰلُهُمۡ فَأَصۡبَحُواْ خَٰسِرِينَ ﴾
[المَائدة: 53]

Ndipo anthu okhulupirira adzati; “Kodi awa ndi anthu omwe analumbira molimbika kuti, pali Mulungu, iwo ali pamodzi ndi inu?” Ntchito zawo zonse zidzakhala zopanda pake ndipo iwo akhala olephera

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ويقول الذين آمنوا أهؤلاء الذين أقسموا بالله جهد أيمانهم إنهم لمعكم حبطت, باللغة نيانجا

﴿ويقول الذين آمنوا أهؤلاء الذين أقسموا بالله جهد أيمانهم إنهم لمعكم حبطت﴾ [المَائدة: 53]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo amene adakhulupirira nayamba kunena (chitaululika chinyengo cha achinyengowo): “Kodi awa si omwe adali kulumbilira dzina la Allah m’kulumbilira kwawo kwamphamvu kuti iwo ali pamodzi ndi inu?” Zochita zawo zaonongeka. Tero akhala otaika
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek