×

Kwa onse amene akhulupirira ndi kuchita zabwino sipadzakhala mlandu pa nkhani ya 5:93 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:93) ayat 93 in Chichewa

5:93 Surah Al-Ma’idah ayat 93 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 93 - المَائدة - Page - Juz 7

﴿لَيۡسَ عَلَى ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ وَعَمِلُواْ ٱلصَّٰلِحَٰتِ جُنَاحٞ فِيمَا طَعِمُوٓاْ إِذَا مَا ٱتَّقَواْ وَّءَامَنُواْ وَعَمِلُواْ ٱلصَّٰلِحَٰتِ ثُمَّ ٱتَّقَواْ وَّءَامَنُواْ ثُمَّ ٱتَّقَواْ وَّأَحۡسَنُواْۚ وَٱللَّهُ يُحِبُّ ٱلۡمُحۡسِنِينَ ﴾
[المَائدة: 93]

Kwa onse amene akhulupirira ndi kuchita zabwino sipadzakhala mlandu pa nkhani ya chakudya chilichonse chimene adadya ngati iwo aopa Mulungu, akhulupirira mwa Iye ndi kuchita ntchito zabwino moyenera. Mulungu amakonda anthu ochita zabwino

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ليس على الذين آمنوا وعملوا الصالحات جناح فيما طعموا إذا ما اتقوا, باللغة نيانجا

﴿ليس على الذين آمنوا وعملوا الصالحات جناح فيما طعموا إذا ما اتقوا﴾ [المَائدة: 93]

Khaled Ibrahim Betala
“Palibe tchimo kwa amene akhulupirira ndi kuchita zabwino pazomwe adadya (zisadaletsedwe) ngati akupitiriza kuopa ndikukhulupirira ndikuchita zabwino; kenako nkuopanso (ataletsedwa zina) ndikukhulupirira; (atalamulidwa zinanso) nkuopanso ndikuchita zabwino. Ndipo Allah, amakonda ochita zabwino
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek