×

Ndithudi anthu onse olakwa adzalandira gawo longa limene anzawo olakwa akale adalandira, 51:59 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Adh-Dhariyat ⮕ (51:59) ayat 59 in Chichewa

51:59 Surah Adh-Dhariyat ayat 59 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Adh-Dhariyat ayat 59 - الذَّاريَات - Page - Juz 27

﴿فَإِنَّ لِلَّذِينَ ظَلَمُواْ ذَنُوبٗا مِّثۡلَ ذَنُوبِ أَصۡحَٰبِهِمۡ فَلَا يَسۡتَعۡجِلُونِ ﴾
[الذَّاريَات: 59]

Ndithudi anthu onse olakwa adzalandira gawo longa limene anzawo olakwa akale adalandira, kotero asandifunse Ine kuchita mofulumira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإن للذين ظلموا ذنوبا مثل ذنوب أصحابهم فلا يستعجلون, باللغة نيانجا

﴿فإن للذين ظلموا ذنوبا مثل ذنوب أصحابهم فلا يستعجلون﴾ [الذَّاريَات: 59]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu amene adzichitira okha chinyengo (pokana ndi kutsutsa) ali nalo gawo la chilango monga gawo la anzawo (a mibadwo yakale); choncho asandifulumizitse (kutsitsa chilango nthawi yake isanafike)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek