×

Dziwani kuti moyo wa padziko lino lapansi ndi masewera ndi wotailako nthawi, 57:20 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hadid ⮕ (57:20) ayat 20 in Chichewa

57:20 Surah Al-hadid ayat 20 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hadid ayat 20 - الحدِيد - Page - Juz 27

﴿ٱعۡلَمُوٓاْ أَنَّمَا ٱلۡحَيَوٰةُ ٱلدُّنۡيَا لَعِبٞ وَلَهۡوٞ وَزِينَةٞ وَتَفَاخُرُۢ بَيۡنَكُمۡ وَتَكَاثُرٞ فِي ٱلۡأَمۡوَٰلِ وَٱلۡأَوۡلَٰدِۖ كَمَثَلِ غَيۡثٍ أَعۡجَبَ ٱلۡكُفَّارَ نَبَاتُهُۥ ثُمَّ يَهِيجُ فَتَرَىٰهُ مُصۡفَرّٗا ثُمَّ يَكُونُ حُطَٰمٗاۖ وَفِي ٱلۡأٓخِرَةِ عَذَابٞ شَدِيدٞ وَمَغۡفِرَةٞ مِّنَ ٱللَّهِ وَرِضۡوَٰنٞۚ وَمَا ٱلۡحَيَوٰةُ ٱلدُّنۡيَآ إِلَّا مَتَٰعُ ٱلۡغُرُورِ ﴾
[الحدِيد: 20]

Dziwani kuti moyo wa padziko lino lapansi ndi masewera ndi wotailako nthawi, chionetsero ndi kunyada ndi mpikisano pakati pa wina ndi mnzake wofuna chuma ndi ana. Fanizo lake lili ngati mvula ndi zomera zimene zimadza chifukwa cha zimene zimabweretsa chisangalalo kwa ozilima. Pasanapite nthawi izo zimafota ndi kuoneka za chikasu. Ndipo zimauma ndi kugwa pansi. Koma m’moyo umene uli kudza, kuli chilango chowawa kwa anthu ogona m’machimo ndi chikhululukiro chochokera kwa Mulungu ndiponso chisangalalo chake kwa iwo amene amadzipereka kwa Mulungu. Kodi moyo wa padziko lino lapansi ndi chiyani kupatula chinyengo chabe

❮ Previous Next ❯

ترجمة: اعلموا أنما الحياة الدنيا لعب ولهو وزينة وتفاخر بينكم وتكاثر في الأموال, باللغة نيانجا

﴿اعلموا أنما الحياة الدنيا لعب ولهو وزينة وتفاخر بينكم وتكاثر في الأموال﴾ [الحدِيد: 20]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek