×

Nena, “Ine ndilibe mphamvu yopeza zinthu, kapena kupewa mavuto kupatula ndi chifuniro 7:188 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:188) ayat 188 in Chichewa

7:188 Surah Al-A‘raf ayat 188 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 188 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿قُل لَّآ أَمۡلِكُ لِنَفۡسِي نَفۡعٗا وَلَا ضَرًّا إِلَّا مَا شَآءَ ٱللَّهُۚ وَلَوۡ كُنتُ أَعۡلَمُ ٱلۡغَيۡبَ لَٱسۡتَكۡثَرۡتُ مِنَ ٱلۡخَيۡرِ وَمَا مَسَّنِيَ ٱلسُّوٓءُۚ إِنۡ أَنَا۠ إِلَّا نَذِيرٞ وَبَشِيرٞ لِّقَوۡمٖ يُؤۡمِنُونَ ﴾
[الأعرَاف: 188]

Nena, “Ine ndilibe mphamvu yopeza zinthu, kapena kupewa mavuto kupatula ndi chifuniro cha Mulungu. Ine ndikadakhala wodziwa chilichonse chobisika ndikadadzichulukitsira chuma ndipo palibe choipa chimene chikadandipeza. Ine sindine wina aliyense ayi koma wopereka chenjezo ndi wobweretsa nkhani yabwino kwa anthu okhulupirira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل لا أملك لنفسي نفعا ولا ضرا إلا ما شاء الله ولو, باللغة نيانجا

﴿قل لا أملك لنفسي نفعا ولا ضرا إلا ما شاء الله ولو﴾ [الأعرَاف: 188]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Ine ndekha ndilibe mphamvu yodzibweretsera chabwino kapena kudzichotsera choipa, koma chimene Allah wafuna. Ndikadakhala kuti ndikudziwa za mseri, ndikadadzichulukitsira zabwino, ndipo choipa sichikadandikhudza. Ine sindili chilichonse koma mchenjezi ndi wouza anthu okhulupirira nkhani zabwino.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek