×

“Ndipo ngati lilipo gulu lina pakati panu limene lidakhulupirira mu Uthenga umene 7:87 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:87) ayat 87 in Chichewa

7:87 Surah Al-A‘raf ayat 87 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 87 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿وَإِن كَانَ طَآئِفَةٞ مِّنكُمۡ ءَامَنُواْ بِٱلَّذِيٓ أُرۡسِلۡتُ بِهِۦ وَطَآئِفَةٞ لَّمۡ يُؤۡمِنُواْ فَٱصۡبِرُواْ حَتَّىٰ يَحۡكُمَ ٱللَّهُ بَيۡنَنَاۚ وَهُوَ خَيۡرُ ٱلۡحَٰكِمِينَ ﴾
[الأعرَاف: 87]

“Ndipo ngati lilipo gulu lina pakati panu limene lidakhulupirira mu Uthenga umene ndidatumizidwa ndi gulu limene silidakhulupirire motero pilira mpaka pamene Mulungu aweruza pakati pathu. Iye ndiye wabwino mwa oweruza onse.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإن كان طائفة منكم آمنوا بالذي أرسلت به وطائفة لم يؤمنوا فاصبروا, باللغة نيانجا

﴿وإن كان طائفة منكم آمنوا بالذي أرسلت به وطائفة لم يؤمنوا فاصبروا﴾ [الأعرَاف: 87]

Khaled Ibrahim Betala
““Ndipo ngati pali gulu la anthu mwa inu amene akhulupirira uthenga umene ndatumidwa nawo, ndi gulu la anthu limene silidakhulupirire, pirirani mpaka Allah aweruze pakati pathu. Iye Ngwabwino poweruza kuposa oweruza.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek