×

Mafumu odzikweza a gulu lina la mtundu wake adati: “Iwe Shaibu! Ndithudi 7:88 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:88) ayat 88 in Chichewa

7:88 Surah Al-A‘raf ayat 88 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 88 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿۞ قَالَ ٱلۡمَلَأُ ٱلَّذِينَ ٱسۡتَكۡبَرُواْ مِن قَوۡمِهِۦ لَنُخۡرِجَنَّكَ يَٰشُعَيۡبُ وَٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ مَعَكَ مِن قَرۡيَتِنَآ أَوۡ لَتَعُودُنَّ فِي مِلَّتِنَاۚ قَالَ أَوَلَوۡ كُنَّا كَٰرِهِينَ ﴾
[الأعرَاف: 88]

Mafumu odzikweza a gulu lina la mtundu wake adati: “Iwe Shaibu! Ndithudi ife tidzakuthamangitsa iwe mu mzinda wathu pamodzi ndi iwo amene akhulupirira ndi iwe kapena kuti mubwerere ku chipembedzo chathu.” Iye adati: “Chiyani! Ngakhale kuti zikutinyansa?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال الملأ الذين استكبروا من قومه لنخرجنك ياشعيب والذين آمنوا معك من, باللغة نيانجا

﴿قال الملأ الذين استكبروا من قومه لنخرجنك ياشعيب والذين آمنوا معك من﴾ [الأعرَاف: 88]

Khaled Ibrahim Betala
“۞ Akuluakulu omwe adadzikuza mwa anthu ake, adanena: “Tikupirikitsa, iwe Shuaib m’mudzi mwathu muno ndi amene akhulupirira pamodzi nawe, pokhapokha mutabwerera ku chipembedzo chathu.” (Iye) adati: “Kodi ngakhale kuti tikuchida?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek