×

“Ngati Inu muwasiya iwo adzasocheretsa akapolo anu okhulupirira ndipo iwo adzabereka anthu 71:27 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Nuh ⮕ (71:27) ayat 27 in Chichewa

71:27 Surah Nuh ayat 27 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Nuh ayat 27 - نُوح - Page - Juz 29

﴿إِنَّكَ إِن تَذَرۡهُمۡ يُضِلُّواْ عِبَادَكَ وَلَا يَلِدُوٓاْ إِلَّا فَاجِرٗا كَفَّارٗا ﴾
[نُوح: 27]

“Ngati Inu muwasiya iwo adzasocheretsa akapolo anu okhulupirira ndipo iwo adzabereka anthu ochita zoipa ndi osakhulupirira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إنك إن تذرهم يضلوا عبادك ولا يلدوا إلا فاجرا كفارا, باللغة نيانجا

﴿إنك إن تذرهم يضلوا عبادك ولا يلدوا إلا فاجرا كفارا﴾ [نُوح: 27]

Khaled Ibrahim Betala
““Ndithu Inu Mbuye wanga ngati muwasiya (popanda kuwaononga ndi kuwathetsa) asokeretsa akapolo anu (kunjira yolungama). Ndipo sangabereke (ana abwino) koma oipa; osakhulupirira (okhala kutali ndi choonadi, ndiponso onyoza Inu).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek