×

Amawateteza mpaka pamene aona kuti iwo apereka uthenga wochokera kwa Ambuye wawo. 72:28 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Jinn ⮕ (72:28) ayat 28 in Chichewa

72:28 Surah Al-Jinn ayat 28 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Jinn ayat 28 - الجِن - Page - Juz 29

﴿لِّيَعۡلَمَ أَن قَدۡ أَبۡلَغُواْ رِسَٰلَٰتِ رَبِّهِمۡ وَأَحَاطَ بِمَا لَدَيۡهِمۡ وَأَحۡصَىٰ كُلَّ شَيۡءٍ عَدَدَۢا ﴾
[الجِن: 28]

Amawateteza mpaka pamene aona kuti iwo apereka uthenga wochokera kwa Ambuye wawo. Ndipo Iye amadziwa chili chonse chimene ali nacho ndipo Iye amasunga chiwerengero cha chinthu chili chonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ليعلم أن قد أبلغوا رسالات ربهم وأحاط بما لديهم وأحصى كل شيء, باللغة نيانجا

﴿ليعلم أن قد أبلغوا رسالات ربهم وأحاط بما لديهم وأحصى كل شيء﴾ [الجِن: 28]

Khaled Ibrahim Betala
““Kuti adziwe ngati afikitsa uthenga wa Mbuye wawo, ndipo wawazungulira (podziwa zonse zili kwa iwo) ndipo wadziwa kuchuluka kwa zinthu zonse zimene zilipo; (palibe chobisika kwa Iye).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek