×

Ndi mmene anthu osakhulupirira adakupangira chiwembu choti akugwire kuti ukhale mndende kapena 8:30 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:30) ayat 30 in Chichewa

8:30 Surah Al-Anfal ayat 30 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 30 - الأنفَال - Page - Juz 9

﴿وَإِذۡ يَمۡكُرُ بِكَ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ لِيُثۡبِتُوكَ أَوۡ يَقۡتُلُوكَ أَوۡ يُخۡرِجُوكَۚ وَيَمۡكُرُونَ وَيَمۡكُرُ ٱللَّهُۖ وَٱللَّهُ خَيۡرُ ٱلۡمَٰكِرِينَ ﴾
[الأنفَال: 30]

Ndi mmene anthu osakhulupirira adakupangira chiwembu choti akugwire kuti ukhale mndende kapena kukupha kapena kukuchotsa m’dziko lako. Iwo amachita chiwembu koma Mulungu, nayenso amakonza chiwembu chake, ndipo Mulungu ndi wopambana pokonza chiwembu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذ يمكر بك الذين كفروا ليثبتوك أو يقتلوك أو يخرجوك ويمكرون ويمكر, باللغة نيانجا

﴿وإذ يمكر بك الذين كفروا ليثبتوك أو يقتلوك أو يخرجوك ويمكرون ويمكر﴾ [الأنفَال: 30]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (kumbukira) pamene omwe sadakhulupirire amakuchitira chiwembu kuti akunjate, kapena akuphe, kapena akutulutse (m’dziko lawo la Makka mwachipongwe). Ndipo amachita chiwembu, naye Allah anawononga chiwembu chawocho. Ndipo Allah ndiwokhoza koposa poononga ziwembu (za anthu oipa)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek