×

Ndipo pakati pawo alipo ena amene amanena zoipa za iwe pa kagawidwe 9:58 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:58) ayat 58 in Chichewa

9:58 Surah At-Taubah ayat 58 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 58 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿وَمِنۡهُم مَّن يَلۡمِزُكَ فِي ٱلصَّدَقَٰتِ فَإِنۡ أُعۡطُواْ مِنۡهَا رَضُواْ وَإِن لَّمۡ يُعۡطَوۡاْ مِنۡهَآ إِذَا هُمۡ يَسۡخَطُونَ ﴾
[التوبَة: 58]

Ndipo pakati pawo alipo ena amene amanena zoipa za iwe pa kagawidwe ka katundu. Ngati iwo atapatsidwa gawo la katunduyo, iwo amasangalala, koma ngati sapatsidwa china chilichonse, amakwiya kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ومنهم من يلمزك في الصدقات فإن أعطوا منها رضوا وإن لم يعطوا, باللغة نيانجا

﴿ومنهم من يلمزك في الصدقات فإن أعطوا منها رضوا وإن لم يعطوا﴾ [التوبَة: 58]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo alipo ena mwa iwo (achiphamaso) amene akukunyogodola mkugawa kwako sadaka. Akapatsidwa kanthu m’menemo amakondwera koma akapanda kupatsidwa akukwiya nawe
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek