×

Iwo amalumbira M’dzina la Mulungu kwa inu kuti akukondweretseni chabe, koma ndi 9:62 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:62) ayat 62 in Chichewa

9:62 Surah At-Taubah ayat 62 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 62 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿يَحۡلِفُونَ بِٱللَّهِ لَكُمۡ لِيُرۡضُوكُمۡ وَٱللَّهُ وَرَسُولُهُۥٓ أَحَقُّ أَن يُرۡضُوهُ إِن كَانُواْ مُؤۡمِنِينَ ﴾
[التوبَة: 62]

Iwo amalumbira M’dzina la Mulungu kwa inu kuti akukondweretseni chabe, koma ndi kwabwino kuti iwo akondweretse Mulungu ndi Mtumwi wake ngati iwo ndi okhulupilira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يحلفون بالله لكم ليرضوكم والله ورسوله أحق أن يرضوه إن كانوا مؤمنين, باللغة نيانجا

﴿يحلفون بالله لكم ليرضوكم والله ورسوله أحق أن يرضوه إن كانوا مؤمنين﴾ [التوبَة: 62]

Khaled Ibrahim Betala
“Akulumbira kwa inu potchula dzina la Allah kuti akukondweretseni (chikhalirecho akunyoza Allah ndi Mtumiki Wake), pomwe Allah ndi Mtumiki Wake ndiye wofunika kuti amkondweretse ngati iwo ngokhulupiriradi (mwachoonadi)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek