×

Kukadakhala kuti munthu aliyense wochita zoipa anali ndi zinthu zonse zimene zili 10:54 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:54) ayat 54 in Chichewa

10:54 Surah Yunus ayat 54 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 54 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَلَوۡ أَنَّ لِكُلِّ نَفۡسٖ ظَلَمَتۡ مَا فِي ٱلۡأَرۡضِ لَٱفۡتَدَتۡ بِهِۦۗ وَأَسَرُّواْ ٱلنَّدَامَةَ لَمَّا رَأَوُاْ ٱلۡعَذَابَۖ وَقُضِيَ بَيۡنَهُم بِٱلۡقِسۡطِ وَهُمۡ لَا يُظۡلَمُونَ ﴾
[يُونس: 54]

Kukadakhala kuti munthu aliyense wochita zoipa anali ndi zinthu zonse zimene zili padziko lapansi ndipo amafuna kuzipereka ngati dipo loti adziombolere, ndipo iwo akanamva chisoni m’mitima yawo pamene akadaona chilango ndipo iwo adzaweruzidwa mwachilungamo ndiponso sadzaponderezedwa ai

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولو أن لكل نفس ظلمت ما في الأرض لافتدت به وأسروا الندامة, باللغة نيانجا

﴿ولو أن لكل نفس ظلمت ما في الأرض لافتدت به وأسروا الندامة﴾ [يُونس: 54]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo kukadakhala kuti munthu aliyense amene adachita zoipa, nkukhala nazo zonse zam’dziko akadapereka zonse kuti adziombole nazo (pamene adzaona kuopsa kwa chilango cha tsikulo). Ndipo akadzachiona chilango, adzayesetsa kubisa madandaulo (awo; koma adzaonekera poyera). Ndipo kudzaweruzidwa mwachilungamo pakati pawo, ndipo iwo sadzaponderezedwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek