×

Akuluakulu osakhulupirira a anthu ake adati, “Munthu uyu ndi wolingana ndi inu, 23:24 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mu’minun ⮕ (23:24) ayat 24 in Chichewa

23:24 Surah Al-Mu’minun ayat 24 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mu’minun ayat 24 - المؤمنُون - Page - Juz 18

﴿فَقَالَ ٱلۡمَلَؤُاْ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ مِن قَوۡمِهِۦ مَا هَٰذَآ إِلَّا بَشَرٞ مِّثۡلُكُمۡ يُرِيدُ أَن يَتَفَضَّلَ عَلَيۡكُمۡ وَلَوۡ شَآءَ ٱللَّهُ لَأَنزَلَ مَلَٰٓئِكَةٗ مَّا سَمِعۡنَا بِهَٰذَا فِيٓ ءَابَآئِنَا ٱلۡأَوَّلِينَ ﴾
[المؤمنُون: 24]

Akuluakulu osakhulupirira a anthu ake adati, “Munthu uyu ndi wolingana ndi inu, iye ali kungodziyenereza kuti ndi wopambana pakati panu.” Mulungu akadafuna, akadatumiza angelo. Ndiponso zinthu za mtundu uwu sitidamvepo kuchokera kwa makolo athu akalekale

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فقال الملأ الذين كفروا من قومه ما هذا إلا بشر مثلكم يريد, باللغة نيانجا

﴿فقال الملأ الذين كفروا من قومه ما هذا إلا بشر مثلكم يريد﴾ [المؤمنُون: 24]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek