×

“Munthu uyu ndi odziyenereza amene ali kunena za Mulungu zimene sizili zoona 23:38 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mu’minun ⮕ (23:38) ayat 38 in Chichewa

23:38 Surah Al-Mu’minun ayat 38 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mu’minun ayat 38 - المؤمنُون - Page - Juz 18

﴿إِنۡ هُوَ إِلَّا رَجُلٌ ٱفۡتَرَىٰ عَلَى ٱللَّهِ كَذِبٗا وَمَا نَحۡنُ لَهُۥ بِمُؤۡمِنِينَ ﴾
[المؤمنُون: 38]

“Munthu uyu ndi odziyenereza amene ali kunena za Mulungu zimene sizili zoona ayi. Ife sitidzamukhulupirira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن هو إلا رجل افترى على الله كذبا وما نحن له بمؤمنين, باللغة نيانجا

﴿إن هو إلا رجل افترى على الله كذبا وما نحن له بمؤمنين﴾ [المؤمنُون: 38]

Khaled Ibrahim Betala
“Uyu saali kanthu (amene akudzitcha kuti ndi Mtumiki) koma ndi munthu basi, akupekera Allah bodza, ndipo ife sitimkhulupirira.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek