×

Ndipo munthu wina adadza kuchokera ku malire a mzinda ali kuthamanga. Iye 28:20 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:20) ayat 20 in Chichewa

28:20 Surah Al-Qasas ayat 20 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 20 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿وَجَآءَ رَجُلٞ مِّنۡ أَقۡصَا ٱلۡمَدِينَةِ يَسۡعَىٰ قَالَ يَٰمُوسَىٰٓ إِنَّ ٱلۡمَلَأَ يَأۡتَمِرُونَ بِكَ لِيَقۡتُلُوكَ فَٱخۡرُجۡ إِنِّي لَكَ مِنَ ٱلنَّٰصِحِينَ ﴾
[القَصَص: 20]

Ndipo munthu wina adadza kuchokera ku malire a mzinda ali kuthamanga. Iye adati, “Mose! Anthu ndi mafumu ali kuchita upo woti akuphe iwe. Tuluka mu mzindawu. Ine ndili kukulangiza iwe mwachoonadi.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وجاء رجل من أقصى المدينة يسعى قال ياموسى إن الملأ يأتمرون بك, باللغة نيانجا

﴿وجاء رجل من أقصى المدينة يسعى قال ياموسى إن الملأ يأتمرون بك﴾ [القَصَص: 20]

Khaled Ibrahim Betala
“(Farawo zitamfika mphekesera kuti Mûsa wapha munthu pothangata mu Israyeli, adalamula kuti Mûsa paliponse pomwe angapezeke, agwidwe ndi kuphedwa). Choncho munthu adadza akuthamanga kuchokera kumalekezero a m’zindawo. Adati: “E iwe Mûsa! Akuluakulu akukuchitira upo kuti akuphe choncho choka (m’dziko muno). Ndithu ine ndine mmodzi mwa okufunira iwe zabwino.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek