×

Ndipo pamene choonadi chadza kwa iwo kuchokera kwa Ife, iwo ali kufunsa 28:48 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:48) ayat 48 in Chichewa

28:48 Surah Al-Qasas ayat 48 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 48 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿فَلَمَّا جَآءَهُمُ ٱلۡحَقُّ مِنۡ عِندِنَا قَالُواْ لَوۡلَآ أُوتِيَ مِثۡلَ مَآ أُوتِيَ مُوسَىٰٓۚ أَوَلَمۡ يَكۡفُرُواْ بِمَآ أُوتِيَ مُوسَىٰ مِن قَبۡلُۖ قَالُواْ سِحۡرَانِ تَظَٰهَرَا وَقَالُوٓاْ إِنَّا بِكُلّٖ كَٰفِرُونَ ﴾
[القَصَص: 48]

Ndipo pamene choonadi chadza kwa iwo kuchokera kwa Ife, iwo ali kufunsa kuti, “Kodi ndi chifukwa chiyani iye sadapatsidwe monga zomwe zidapatsidwa kwa Mose?” Kodi iwo sadakane zimene zidapatsidwa kwa Mose kale? Iwo amati, “Zizindikiro ziwiri za matsenga zili zothandizana.” Ndiponso amanena, “Ife sitidzakhulupirira mu china chilichonse cha zimenezi.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما جاءهم الحق من عندنا قالوا لولا أوتي مثل ما أوتي موسى, باللغة نيانجا

﴿فلما جاءهم الحق من عندنا قالوا لولا أوتي مثل ما أوتي موسى﴾ [القَصَص: 48]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma choona pamene chidawadzera kuchokera kwa Ife, adati: “Bwanji sadapatsidwe zonga zomwe adapatsidwa Mûsa? (Monga kutembenuza ndodo kukhala njoka, ndi zina zotero).” Kodi kalelo sadazikane zomwe adapatsidwa Mûsa? Nkunena (za Taurati ndi Qur’an): “Ndimatsenga awiri amene akuthandizana.” Ndipo adati: “Ndithu ife tikuwakana onse.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek