×

Ife tidzaika mantha m’mitima ya anthu osakhulupirira chifukwa amatumikira milungu ina yowojezera 3:151 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:151) ayat 151 in Chichewa

3:151 Surah al-‘Imran ayat 151 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 151 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿سَنُلۡقِي فِي قُلُوبِ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ ٱلرُّعۡبَ بِمَآ أَشۡرَكُواْ بِٱللَّهِ مَا لَمۡ يُنَزِّلۡ بِهِۦ سُلۡطَٰنٗاۖ وَمَأۡوَىٰهُمُ ٱلنَّارُۖ وَبِئۡسَ مَثۡوَى ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[آل عِمران: 151]

Ife tidzaika mantha m’mitima ya anthu osakhulupirira chifukwa amatumikira milungu ina yowojezera pa Mulungu imene iwo sadalandire chilolezo choti azitumikira. Moto udzakhala mudzi wawo. Ndithu onyansa kwambiri ndi malo amene anthu ochita zoipa akakhalako

❮ Previous Next ❯

ترجمة: سنلقي في قلوب الذين كفروا الرعب بما أشركوا بالله ما لم ينـزل, باللغة نيانجا

﴿سنلقي في قلوب الذين كفروا الرعب بما أشركوا بالله ما لم ينـزل﴾ [آل عِمران: 151]

Khaled Ibrahim Betala
“Tiponya mantha m’mitima mwa amene sadakhulupirire chifukwa chakumphatikiza Allah (ndi mafano) omwe Allah sadatsitsire umboni (wosonyeza umulungu wawo) ndipo malo awo adzakhala ku Moto. Taonani kuipitsitsa malo a anthu ochita zoipa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek