×

Ndithudi iwo amene sanakhulupirire, ndipo akufa ali osakhulupirira, machimo awo sadzakhululukidwa ngakhale 3:91 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:91) ayat 91 in Chichewa

3:91 Surah al-‘Imran ayat 91 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 91 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿إِنَّ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ وَمَاتُواْ وَهُمۡ كُفَّارٞ فَلَن يُقۡبَلَ مِنۡ أَحَدِهِم مِّلۡءُ ٱلۡأَرۡضِ ذَهَبٗا وَلَوِ ٱفۡتَدَىٰ بِهِۦٓۗ أُوْلَٰٓئِكَ لَهُمۡ عَذَابٌ أَلِيمٞ وَمَا لَهُم مِّن نَّٰصِرِينَ ﴾
[آل عِمران: 91]

Ndithudi iwo amene sanakhulupirire, ndipo akufa ali osakhulupirira, machimo awo sadzakhululukidwa ngakhale atapereka golide wodzadza dziko lonse lapansi ngati chodziombolera. Kwa otero, chilango chowawa chili kuwadikira ndipo iwo sadzapeza aliyense owathandiza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الذين كفروا وماتوا وهم كفار فلن يقبل من أحدهم ملء الأرض, باللغة نيانجا

﴿إن الذين كفروا وماتوا وهم كفار فلن يقبل من أحدهم ملء الأرض﴾ [آل عِمران: 91]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithudi amene sadakhulupirire, nkumwalira pamene ali osakhulupirira, sikudzalandiridwa kwa aliyense wa iwo ngakhale atapereka dipo la golide lodzadza dziko lonse. Iwo ndi omwe adzalandire chilango chopweteka, ndipo sadzakhala ndi athandizi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek