×

Ndipo Mulungu akamalanga anthu chifukwa cha zoipa zimene amachita, sipakadakhala cholengedwa chimene 35:45 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah FaTir ⮕ (35:45) ayat 45 in Chichewa

35:45 Surah FaTir ayat 45 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah FaTir ayat 45 - فَاطِر - Page - Juz 22

﴿وَلَوۡ يُؤَاخِذُ ٱللَّهُ ٱلنَّاسَ بِمَا كَسَبُواْ مَا تَرَكَ عَلَىٰ ظَهۡرِهَا مِن دَآبَّةٖ وَلَٰكِن يُؤَخِّرُهُمۡ إِلَىٰٓ أَجَلٖ مُّسَمّٗىۖ فَإِذَا جَآءَ أَجَلُهُمۡ فَإِنَّ ٱللَّهَ كَانَ بِعِبَادِهِۦ بَصِيرَۢا ﴾
[فَاطِر: 45]

Ndipo Mulungu akamalanga anthu chifukwa cha zoipa zimene amachita, sipakadakhala cholengedwa chimene chikadakhala ndi moyo padziko lapansi. Koma Iye amazisunga mpaka pa nthawi ya malire awo. Ndipo pamene nthawi yawo ikwana, ndithudi, Mulungu amaona akapolo ake onse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولو يؤاخذ الله الناس بما كسبوا ما ترك على ظهرها من دابة, باللغة نيانجا

﴿ولو يؤاخذ الله الناس بما كسبوا ما ترك على ظهرها من دابة﴾ [فَاطِر: 45]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Allah akadamalanga anthu chifukwa cha zomwe alakwa, sakadasiya pamwamba pake (pa nthaka) chamoyo chilichonse; koma Iye amawalekelera mpaka nthawi yomwe adaiikayo. Choncho nthawi yawo ikadzawadzera, (pompo adzalangidwa). Ndithu Allah akuwadziwa bwino akapolo Ake
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek