×

Ndipo Ife sitidatumize padziko lapansi, kwa anthu ake, gulu lochokera kumwamba kuti 36:28 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ya-Sin ⮕ (36:28) ayat 28 in Chichewa

36:28 Surah Ya-Sin ayat 28 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ya-Sin ayat 28 - يسٓ - Page - Juz 23

﴿۞ وَمَآ أَنزَلۡنَا عَلَىٰ قَوۡمِهِۦ مِنۢ بَعۡدِهِۦ مِن جُندٖ مِّنَ ٱلسَّمَآءِ وَمَا كُنَّا مُنزِلِينَ ﴾
[يسٓ: 28]

Ndipo Ife sitidatumize padziko lapansi, kwa anthu ake, gulu lochokera kumwamba kuti lilimbane nawo ndipo sikudali koyenera kuti Ife tichite choncho

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما أنـزلنا على قومه من بعده من جند من السماء وما كنا, باللغة نيانجا

﴿وما أنـزلنا على قومه من بعده من جند من السماء وما كنا﴾ [يسٓ: 28]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo anthu ake sitidawatsitsire ankhondo ochokera kumwamba pambuyo pake (kuti awaononge). Ndipo pachizolowezi chathu sititsitsa (ankhondo kumwamba tikafuna kuononga, koma Mngelo mmodzi amakwanira)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek