×

Ngati inu simukhulupirira, ndithudi, muyenera kudziwa kuti Mulungu ndi woima payekha ndipo 39:7 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:7) ayat 7 in Chichewa

39:7 Surah Az-Zumar ayat 7 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 7 - الزُّمَر - Page - Juz 23

﴿إِن تَكۡفُرُواْ فَإِنَّ ٱللَّهَ غَنِيٌّ عَنكُمۡۖ وَلَا يَرۡضَىٰ لِعِبَادِهِ ٱلۡكُفۡرَۖ وَإِن تَشۡكُرُواْ يَرۡضَهُ لَكُمۡۗ وَلَا تَزِرُ وَازِرَةٞ وِزۡرَ أُخۡرَىٰۚ ثُمَّ إِلَىٰ رَبِّكُم مَّرۡجِعُكُمۡ فَيُنَبِّئُكُم بِمَا كُنتُمۡ تَعۡمَلُونَۚ إِنَّهُۥ عَلِيمُۢ بِذَاتِ ٱلصُّدُورِ ﴾
[الزُّمَر: 7]

Ngati inu simukhulupirira, ndithudi, muyenera kudziwa kuti Mulungu ndi woima payekha ndipo alibe nanu kanthu ayi. Iye sakonda kusakhulupirira kwa akapolo ake. Koma ngati inu muthokoza, Iye amasangalala nanu. Ndipo palibe munthu amene adzasenza katundu wa mnzake. Ndipo ndi kwa Ambuye wanu kumene nonse mudzabwerera. Ndipo Iye adzakuuzani zonse zimene mudachita. Ndithudi Iye amadziwa chilichonse chimene chili m’mitima mwanu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن تكفروا فإن الله غني عنكم ولا يرضى لعباده الكفر وإن تشكروا, باللغة نيانجا

﴿إن تكفروا فإن الله غني عنكم ولا يرضى لعباده الكفر وإن تشكروا﴾ [الزُّمَر: 7]

Khaled Ibrahim Betala
“Ngati mukana ndithu Allah Ngodzikwaniritsa sasaukira kwa inu (chikhulupiliro chanu ndi kuthokoza kwanu); koma sakonda kukanira kwa anthu Ake. Ngati mumthokoza (pa mtendere Wake umene uli pa inu) akuyanja kuthokoza kwanuko. Ndipo mzimu wochimwa sungasenze machimo a mzimu wina. Kenako kobwerera kwanu nkwa Mbuye wanu, ndipo adzakuuzani zimene mudali kuchita. Ndithu Iye Ngodziwa (zinsinsi) za m’mitima
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek