×

Koma iwo amene amakhulupirira ndi kuchita ntchito zabwino, Ife tidzawalowetsa m’minda yothiriridwa 4:57 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:57) ayat 57 in Chichewa

4:57 Surah An-Nisa’ ayat 57 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 57 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿وَٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ وَعَمِلُواْ ٱلصَّٰلِحَٰتِ سَنُدۡخِلُهُمۡ جَنَّٰتٖ تَجۡرِي مِن تَحۡتِهَا ٱلۡأَنۡهَٰرُ خَٰلِدِينَ فِيهَآ أَبَدٗاۖ لَّهُمۡ فِيهَآ أَزۡوَٰجٞ مُّطَهَّرَةٞۖ وَنُدۡخِلُهُمۡ ظِلّٗا ظَلِيلًا ﴾
[النِّسَاء: 57]

Koma iwo amene amakhulupirira ndi kuchita ntchito zabwino, Ife tidzawalowetsa m’minda yothiriridwa ndi mitsinje yoyenda pansi pake, ndipo adzakhalako mpaka kalekale. Ndipo kumeneko adzakhala ndi akazi oyera ndipo Ife tidzawalowetsa ku mthunzi wabwino kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: والذين آمنوا وعملوا الصالحات سندخلهم جنات تجري من تحتها الأنهار خالدين فيها, باللغة نيانجا

﴿والذين آمنوا وعملوا الصالحات سندخلهم جنات تجري من تحتها الأنهار خالدين فيها﴾ [النِّسَاء: 57]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo amene akhulupirira ndi kuchita zabwino, Tidzawalowetsa m’minda momwe mitsinje ikuyenda pansi (ndi patsogolo) pake. Adzakhala mmenemo muyaya. Ndipo iwo adzapeza mmenemo akazi oyeretsedwa (ku uve wamtundu uliwonse) ndi kuwalowetsa ku mithunzi yabwino kwambiri
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek