×

Ndithudi! Iwo amene angelo amachotsa moyo wawo pamene ali ochimwa, adzafunsidwa kuti: 4:97 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:97) ayat 97 in Chichewa

4:97 Surah An-Nisa’ ayat 97 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 97 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿إِنَّ ٱلَّذِينَ تَوَفَّىٰهُمُ ٱلۡمَلَٰٓئِكَةُ ظَالِمِيٓ أَنفُسِهِمۡ قَالُواْ فِيمَ كُنتُمۡۖ قَالُواْ كُنَّا مُسۡتَضۡعَفِينَ فِي ٱلۡأَرۡضِۚ قَالُوٓاْ أَلَمۡ تَكُنۡ أَرۡضُ ٱللَّهِ وَٰسِعَةٗ فَتُهَاجِرُواْ فِيهَاۚ فَأُوْلَٰٓئِكَ مَأۡوَىٰهُمۡ جَهَنَّمُۖ وَسَآءَتۡ مَصِيرًا ﴾
[النِّسَاء: 97]

Ndithudi! Iwo amene angelo amachotsa moyo wawo pamene ali ochimwa, adzafunsidwa kuti: “Mudali kuchita chiyani?” Iwo adzanena: “Tinali opanda mphamvu ndi oponderezedwa padziko lapansi.” Angelo adzati kwa iwo: “Kodi dziko la Mulungu silinali lotambasuka kuti inu mukadasamuka?” Iwo mudzi wawo ndi Gahena. Malo oipa kwambiri ofikirako

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الذين توفاهم الملائكة ظالمي أنفسهم قالوا فيم كنتم قالوا كنا مستضعفين, باللغة نيانجا

﴿إن الذين توفاهم الملائكة ظالمي أنفسهم قالوا فيم كنتم قالوا كنا مستضعفين﴾ [النِّسَاء: 97]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithudi amene angelo atenga miyoyo yawo, ali odzichitira okha zoipa (posasamuka ku Makka), adzawauza kuti: “Mudachitanji (pachipembedzo chanu?)” Iwo adzati: “Tidali ofooka ndi oponderezedwa padziko; (choncho sitidathe kuchita mapemphero athu).” (Angelo) adzati: “Kodi dziko la Allah silidali lotambasuka kotero kuti inu nkusamukira kwina m’menemo?” Iwowo malo awo ndi Jahannam. Taonani kuipa kwa malo obwerera
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek