×

Ndipo Mose adati, “Ndithudi ine ndithawira kwa Ambuye wanga ndi Ambuye wanu 40:27 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ghafir ⮕ (40:27) ayat 27 in Chichewa

40:27 Surah Ghafir ayat 27 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ghafir ayat 27 - غَافِر - Page - Juz 24

﴿وَقَالَ مُوسَىٰٓ إِنِّي عُذۡتُ بِرَبِّي وَرَبِّكُم مِّن كُلِّ مُتَكَبِّرٖ لَّا يُؤۡمِنُ بِيَوۡمِ ٱلۡحِسَابِ ﴾
[غَافِر: 27]

Ndipo Mose adati, “Ndithudi ine ndithawira kwa Ambuye wanga ndi Ambuye wanu kuti anditeteze kwa aliyense wamwano amene sakhulupirira mu tsiku lachiweruzo.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقال موسى إني عذت بربي وربكم من كل متكبر لا يؤمن بيوم, باللغة نيانجا

﴿وقال موسى إني عذت بربي وربكم من كل متكبر لا يؤمن بيوم﴾ [غَافِر: 27]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Mûsa adati (kwa Farawo pa modzi ndi anthu ake): “Ine ndadzitchinjiriza ndi Mbuye wanga amenenso ali Mbuye wanu (ku chiwembu) chochokera kwa aliyense wodzikweza, wosakhulupirira za tsiku la chiwerengero
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek