×

“Oh inu anthu anga! Moyo wa pa dziko lino ndi chisangalalo cha 40:39 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ghafir ⮕ (40:39) ayat 39 in Chichewa

40:39 Surah Ghafir ayat 39 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ghafir ayat 39 - غَافِر - Page - Juz 24

﴿يَٰقَوۡمِ إِنَّمَا هَٰذِهِ ٱلۡحَيَوٰةُ ٱلدُّنۡيَا مَتَٰعٞ وَإِنَّ ٱلۡأٓخِرَةَ هِيَ دَارُ ٱلۡقَرَارِ ﴾
[غَافِر: 39]

“Oh inu anthu anga! Moyo wa pa dziko lino ndi chisangalalo cha kanthawi kochepa ndipo, ndithudi, moyo umene uli nkudza ndi wosatha.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياقوم إنما هذه الحياة الدنيا متاع وإن الآخرة هي دار القرار, باللغة نيانجا

﴿ياقوم إنما هذه الحياة الدنيا متاع وإن الآخرة هي دار القرار﴾ [غَافِر: 39]

Khaled Ibrahim Betala
““E inu anthu anga! Ndithu moyo wa pa dziko lapansi ndichisangalalo (chakutha). Ndithu tsiku lachimaliziro ndiye nyumba yokhazikikamo.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek