×

Koma chikhulupiriro chawo sichidawathandize china chilichonse pamene adaona chilango chathu. Ili ndi 40:85 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ghafir ⮕ (40:85) ayat 85 in Chichewa

40:85 Surah Ghafir ayat 85 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ghafir ayat 85 - غَافِر - Page - Juz 24

﴿فَلَمۡ يَكُ يَنفَعُهُمۡ إِيمَٰنُهُمۡ لَمَّا رَأَوۡاْ بَأۡسَنَاۖ سُنَّتَ ٱللَّهِ ٱلَّتِي قَدۡ خَلَتۡ فِي عِبَادِهِۦۖ وَخَسِرَ هُنَالِكَ ٱلۡكَٰفِرُونَ ﴾
[غَافِر: 85]

Koma chikhulupiriro chawo sichidawathandize china chilichonse pamene adaona chilango chathu. Ili ndi lamulo la Mulungu limene amaweruzira akapolo ake. Ndipo pamenepo, anthu okana Mulungu adatayika kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلم يك ينفعهم إيمانهم لما رأوا بأسنا سنة الله التي قد خلت, باللغة نيانجا

﴿فلم يك ينفعهم إيمانهم لما رأوا بأسنا سنة الله التي قد خلت﴾ [غَافِر: 85]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma chikhulupiliro chawo sichidali chowathandiza panthawi imeneyo, pomwe adali atachiona kale chilango Chathu. Ichi ndi chizolowezi cha Allah chomwe chidapita pa akapolo (Ake onse kuti chilango chikadza, kulapa sikuvomerezedwa). Choncho pamenepo, okanira adaluza
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek