×

Motero chilichonse chimene mwapatsidwa padziko lapansindichongosangalatsacham’moyounokomachimene chilindi Mulungundichabwinondiponsochosathakwaiwo amene amakhulupirira ndipo amaika 42:36 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:36) ayat 36 in Chichewa

42:36 Surah Ash-Shura ayat 36 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 36 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿فَمَآ أُوتِيتُم مِّن شَيۡءٖ فَمَتَٰعُ ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَاۚ وَمَا عِندَ ٱللَّهِ خَيۡرٞ وَأَبۡقَىٰ لِلَّذِينَ ءَامَنُواْ وَعَلَىٰ رَبِّهِمۡ يَتَوَكَّلُونَ ﴾
[الشُّوري: 36]

Motero chilichonse chimene mwapatsidwa padziko lapansindichongosangalatsacham’moyounokomachimene chilindi Mulungundichabwinondiponsochosathakwaiwo amene amakhulupirira ndipo amaika chikhulupiriro chawo mwa Ambuye wawo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فما أوتيتم من شيء فمتاع الحياة الدنيا وما عند الله خير وأبقى, باللغة نيانجا

﴿فما أوتيتم من شيء فمتاع الحياة الدنيا وما عند الله خير وأبقى﴾ [الشُّوري: 36]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo chilichonse chimene mwapatsidwa, nzosangalatsa za moyo wa pa dziko. Koma zimene zili kwa Allah ndi zabwino ndiponso zamuyaya za amene akhulupirira ndi kutsamira kwa Mbuye wawo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek