×

Mlandu uli pa iwo amene amapondereza anthu pochita zoipa ndipo mwamwano amaswa 42:42 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:42) ayat 42 in Chichewa

42:42 Surah Ash-Shura ayat 42 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 42 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿إِنَّمَا ٱلسَّبِيلُ عَلَى ٱلَّذِينَ يَظۡلِمُونَ ٱلنَّاسَ وَيَبۡغُونَ فِي ٱلۡأَرۡضِ بِغَيۡرِ ٱلۡحَقِّۚ أُوْلَٰٓئِكَ لَهُمۡ عَذَابٌ أَلِيمٞ ﴾
[الشُّوري: 42]

Mlandu uli pa iwo amene amapondereza anthu pochita zoipa ndipo mwamwano amaswa malamulo mopyola muyeso padziko. Ndipo kwa otere kudzakhala chilango chowawa kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إنما السبيل على الذين يظلمون الناس ويبغون في الأرض بغير الحق أولئك, باللغة نيانجا

﴿إنما السبيل على الذين يظلمون الناس ويبغون في الأرض بغير الحق أولئك﴾ [الشُّوري: 42]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu njira yodzudzulidwira ili kwa amene akupondereza anthu ndi kuchita mtopola pa dziko popanda chifukwa choyenera. Iwowo ndi amene adzalandira chilango chowawa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek