×

Abwenzi patsiku limeneli adzasanduka adani kupatula okhawo amene amalewa zoipa 43:67 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zukhruf ⮕ (43:67) ayat 67 in Chichewa

43:67 Surah Az-Zukhruf ayat 67 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zukhruf ayat 67 - الزُّخرُف - Page - Juz 25

﴿ٱلۡأَخِلَّآءُ يَوۡمَئِذِۭ بَعۡضُهُمۡ لِبَعۡضٍ عَدُوٌّ إِلَّا ٱلۡمُتَّقِينَ ﴾
[الزُّخرُف: 67]

Abwenzi patsiku limeneli adzasanduka adani kupatula okhawo amene amalewa zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الأخلاء يومئذ بعضهم لبعض عدو إلا المتقين, باللغة نيانجا

﴿الأخلاء يومئذ بعضهم لبعض عدو إلا المتقين﴾ [الزُّخرُف: 67]

Khaled Ibrahim Betala
“Abwenzi tsiku limenelo adzakhala odana, wina ndi mnzake, (chifukwa chakuti adali kuthandizana pa zinthu zosalungama ndi zamachimo) kupatula oopa Allah (amene adachita chibwenzi mwa Allah, pothandizana kukwaniritsa malamulo a Allah ndi kusiya zimene Allah waletsa)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek