×

Ndithudi iwo sangakuthandize chilichonse ku mkwiyo wa Mulungu. Ndi anthu oipa okha 45:19 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Jathiyah ⮕ (45:19) ayat 19 in Chichewa

45:19 Surah Al-Jathiyah ayat 19 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Jathiyah ayat 19 - الجاثِية - Page - Juz 25

﴿إِنَّهُمۡ لَن يُغۡنُواْ عَنكَ مِنَ ٱللَّهِ شَيۡـٔٗاۚ وَإِنَّ ٱلظَّٰلِمِينَ بَعۡضُهُمۡ أَوۡلِيَآءُ بَعۡضٖۖ وَٱللَّهُ وَلِيُّ ٱلۡمُتَّقِينَ ﴾
[الجاثِية: 19]

Ndithudi iwo sangakuthandize chilichonse ku mkwiyo wa Mulungu. Ndi anthu oipa okha okha omwe amakhala ngati atetezi a wina ndi mnzake koma Mulungu ndi Mtetezi wa iwo amene amalewa zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إنهم لن يغنوا عنك من الله شيئا وإن الظالمين بعضهم أولياء بعض, باللغة نيانجا

﴿إنهم لن يغنوا عنك من الله شيئا وإن الظالمين بعضهم أولياء بعض﴾ [الجاثِية: 19]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu iwo (amene akutsata njira zonama) sangakuthandize chilichonse kwa Allah; ndithu achinyengo ena a iwo amatetezana wina ndi nzake; koma Allah ndi Mtetezi wa oopa (Iye potsatira malamulo Ake ndi kusiya zoletsedwa)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek