×

Ndipo pamene adachiona icho ngati mtambo woyera kuchokera kumwamba kupita ku madambo, 46:24 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahqaf ⮕ (46:24) ayat 24 in Chichewa

46:24 Surah Al-Ahqaf ayat 24 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahqaf ayat 24 - الأحقَاف - Page - Juz 26

﴿فَلَمَّا رَأَوۡهُ عَارِضٗا مُّسۡتَقۡبِلَ أَوۡدِيَتِهِمۡ قَالُواْ هَٰذَا عَارِضٞ مُّمۡطِرُنَاۚ بَلۡ هُوَ مَا ٱسۡتَعۡجَلۡتُم بِهِۦۖ رِيحٞ فِيهَا عَذَابٌ أَلِيمٞ ﴾
[الأحقَاف: 24]

Ndipo pamene adachiona icho ngati mtambo woyera kuchokera kumwamba kupita ku madambo, iwo adati, “Uwu ndi mtambo umene udzatibweretsera ife mvula.” “Iyayi. Ili ndi tsoka limene mumafuna kuti lidze msanga kwa inu. Ndi mphepo ya mkuntho m’mene muli chilango choopsa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما رأوه عارضا مستقبل أوديتهم قالوا هذا عارض ممطرنا بل هو ما, باللغة نيانجا

﴿فلما رأوه عارضا مستقبل أوديتهم قالوا هذا عارض ممطرنا بل هو ما﴾ [الأحقَاف: 24]

Khaled Ibrahim Betala
“Kenako pamene adauona (mtambo) ukulunjika ku zigwa zawo, adanena: “(Mtambo) uwu ndi wotivumbwitsira mvula!” (Adauzidwa): “Iyayi, chimenechi ndichimene mudachifulumizitsa chija (kuti chidze mwachangu), mphepo (ya mkutho) yomwe mkati mwake muli chilango chowawa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek