×

Kapena iwo amati, “Wapeka yekha?” Nena, “Ngati ine ndapeka ndekha, inu mulibe 46:8 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahqaf ⮕ (46:8) ayat 8 in Chichewa

46:8 Surah Al-Ahqaf ayat 8 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahqaf ayat 8 - الأحقَاف - Page - Juz 26

﴿أَمۡ يَقُولُونَ ٱفۡتَرَىٰهُۖ قُلۡ إِنِ ٱفۡتَرَيۡتُهُۥ فَلَا تَمۡلِكُونَ لِي مِنَ ٱللَّهِ شَيۡـًٔاۖ هُوَ أَعۡلَمُ بِمَا تُفِيضُونَ فِيهِۚ كَفَىٰ بِهِۦ شَهِيدَۢا بَيۡنِي وَبَيۡنَكُمۡۖ وَهُوَ ٱلۡغَفُورُ ٱلرَّحِيمُ ﴾
[الأحقَاف: 8]

Kapena iwo amati, “Wapeka yekha?” Nena, “Ngati ine ndapeka ndekha, inu mulibe mphamvu yonditeteza ine kwa Mulungu. Iye ali kudziwa bwino chilichonse chimene mumanena chokhudza chimenechi. Iye ndi wokwana kukhala mboni pakati pa ine ndi inu ndipo Iye ndi wokhululukira ndiponso Mwini chisoni chosatha.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أم يقولون افتراه قل إن افتريته فلا تملكون لي من الله شيئا, باللغة نيانجا

﴿أم يقولون افتراه قل إن افتريته فلا تملكون لي من الله شيئا﴾ [الأحقَاف: 8]

Khaled Ibrahim Betala
“Kapena akunena kuti: “Waipeka (Qur’an)?” Nena: “Ngati ine ndaipeka, tero simungapeze chondithandizira nacho kwa Allah (ku chilango Chake). Iye ndiwodziwa kwambiri zimene mukuzijijirikira. Iye akukwana kukhala mboni pakati pa ine ndi inu ndipo Iye Ngokhululuka kwabasi, Wachisoni chosatha.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek