×

Ndipo mwa anthu a Thamoud. Pamene adauzidwa kuti, “Basangalalani kanthawi kochepa.” 51:43 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Adh-Dhariyat ⮕ (51:43) ayat 43 in Chichewa

51:43 Surah Adh-Dhariyat ayat 43 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Adh-Dhariyat ayat 43 - الذَّاريَات - Page - Juz 27

﴿وَفِي ثَمُودَ إِذۡ قِيلَ لَهُمۡ تَمَتَّعُواْ حَتَّىٰ حِينٖ ﴾
[الذَّاريَات: 43]

Ndipo mwa anthu a Thamoud. Pamene adauzidwa kuti, “Basangalalani kanthawi kochepa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وفي ثمود إذ قيل لهم تمتعوا حتى حين, باللغة نيانجا

﴿وفي ثمود إذ قيل لهم تمتعوا حتى حين﴾ [الذَّاريَات: 43]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo m’nkhani ya Samudu (muli chisonyezo) pamene kudanenedwa kwa iwo kuti: “Sangalalani (mnyumba zanu) mpaka nthawi yaikika.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek