×

Kuti anthu a m’Buku adziwe kuti iwo alibe mphamvu ina iliyonse pa 57:29 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hadid ⮕ (57:29) ayat 29 in Chichewa

57:29 Surah Al-hadid ayat 29 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hadid ayat 29 - الحدِيد - Page - Juz 27

﴿لِّئَلَّا يَعۡلَمَ أَهۡلُ ٱلۡكِتَٰبِ أَلَّا يَقۡدِرُونَ عَلَىٰ شَيۡءٖ مِّن فَضۡلِ ٱللَّهِ وَأَنَّ ٱلۡفَضۡلَ بِيَدِ ٱللَّهِ يُؤۡتِيهِ مَن يَشَآءُۚ وَٱللَّهُ ذُو ٱلۡفَضۡلِ ٱلۡعَظِيمِ ﴾
[الحدِيد: 29]

Kuti anthu a m’Buku adziwe kuti iwo alibe mphamvu ina iliyonse pa chisomo cha Mulungu ndipo kuti chisomo chake chili m’manja mwake mokha ndipo amachipereka kwa aliyense amene Iye wamufuna. Mulungu ndiye Mwini mphatso zosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لئلا يعلم أهل الكتاب ألا يقدرون على شيء من فضل الله وأن, باللغة نيانجا

﴿لئلا يعلم أهل الكتاب ألا يقدرون على شيء من فضل الله وأن﴾ [الحدِيد: 29]

Khaled Ibrahim Betala
“(Allah akupatsani zonsezi) kuti adziwe amene adapatsidwa buku (omwe sadamkhulupirire Mtumiki{s.a.w}) kuti iwo sangathe kudzisankhira okha chilichonse mu mtendere wa Allah. Ndipo ndithu ubwino wonse uli m’manja mwa Allah Yekha. Amapatsa amene wamfuna mwa akapolo Ake. Ndipo Allah ndi Mwini ubwino wochuluka
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek