×

Ndithudi iwo amene ali ndi Ambuye wako sanyada pogwira ntchito yopembedza Mulungu 7:206 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:206) ayat 206 in Chichewa

7:206 Surah Al-A‘raf ayat 206 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 206 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿إِنَّ ٱلَّذِينَ عِندَ رَبِّكَ لَا يَسۡتَكۡبِرُونَ عَنۡ عِبَادَتِهِۦ وَيُسَبِّحُونَهُۥ وَلَهُۥ يَسۡجُدُونَۤ۩ ﴾
[الأعرَاف: 206]

Ndithudi iwo amene ali ndi Ambuye wako sanyada pogwira ntchito yopembedza Mulungu koma amamulemekeza Iye ndipo amagunditsa phumi zawo pamaso pake

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الذين عند ربك لا يستكبرون عن عبادته ويسبحونه وله يسجدون, باللغة نيانجا

﴿إن الذين عند ربك لا يستكبرون عن عبادته ويسبحونه وله يسجدون﴾ [الأعرَاف: 206]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu amene ali kwa Mbuye wako, (angelo), sadzitukumula posiya kumpembedza (Mbuye wawo, koma iwo) amam’lemekeza ndi kumlambira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek