×

Ndipo Ife sitimatumiza Mtumwi ku mzinda wina uli wonse koma timagwetsa pa 7:94 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:94) ayat 94 in Chichewa

7:94 Surah Al-A‘raf ayat 94 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 94 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿وَمَآ أَرۡسَلۡنَا فِي قَرۡيَةٖ مِّن نَّبِيٍّ إِلَّآ أَخَذۡنَآ أَهۡلَهَا بِٱلۡبَأۡسَآءِ وَٱلضَّرَّآءِ لَعَلَّهُمۡ يَضَّرَّعُونَ ﴾
[الأعرَاف: 94]

Ndipo Ife sitimatumiza Mtumwi ku mzinda wina uli wonse koma timagwetsa pa anthu ake umphawi, matenda ndi matsoka kuti akhoza kudzichepetsa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما أرسلنا في قرية من نبي إلا أخذنا أهلها بالبأساء والضراء لعلهم, باللغة نيانجا

﴿وما أرسلنا في قرية من نبي إلا أخذنا أهلها بالبأساء والضراء لعلهم﴾ [الأعرَاف: 94]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo palibe pamene tidamtuma mneneri aliyense m’mudzi uliwonse (nkumukana) koma tinkawalanga eni mudziwo ndi masautso ndi mavuto kuti afatse (ndi kulambira Allah; koma ayi adakanika)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek