القرآن باللغة نيانجا - سورة القارعة مترجمة إلى اللغة نيانجا، Surah Qariah in Chichewa. نوفر ترجمة دقيقة سورة القارعة باللغة نيانجا - Chichewa, الآيات 11 - رقم السورة 101 - الصفحة 600.

| الْقَارِعَةُ (1) Tsiku louka kwa akufa |
| مَا الْقَارِعَةُ (2) Kodi tsiku louka kwa akufa ndi chiyani |
| وَمَا أَدْرَاكَ مَا الْقَارِعَةُ (3) Kodi ndi chiyani chimene chidzakuuze iwe kuti tsiku louka kwa akufa ndi chiani |
| يَوْمَ يَكُونُ النَّاسُ كَالْفَرَاشِ الْمَبْثُوثِ (4) Ndi tsiku limene anthu adzakhala ngati dzombe louluka paliponse |
| وَتَكُونُ الْجِبَالُ كَالْعِهْنِ الْمَنفُوشِ (5) Ndi mapiri adzakhala ngati fumbefumbe za ubweya |
| فَأَمَّا مَن ثَقُلَتْ مَوَازِينُهُ (6) Ndipo iye amene muyeso wake wa ntchito zabwino udzakhala wolemera |
| فَهُوَ فِي عِيشَةٍ رَّاضِيَةٍ (7) Adzakhala ndi moyo wa chimwemwe ndi chisangalalo |
| وَأَمَّا مَنْ خَفَّتْ مَوَازِينُهُ (8) Koma iye amene muyeso wake wa ntchito zabwino udzapezeka wopepuka |
| فَأُمُّهُ هَاوِيَةٌ (9) Mudzi wake udzakhala dzenje lamoto |
| وَمَا أَدْرَاكَ مَا هِيَهْ (10) Kodi ndi chiyani chimene chidzakuuze zinthu zonsezi |
| نَارٌ حَامِيَةٌ (11) Ndi moto wa malawi osatha |