القرآن باللغة نيانجا - سورة الزلزلة مترجمة إلى اللغة نيانجا، Surah Zalzalah in Chichewa. نوفر ترجمة دقيقة سورة الزلزلة باللغة نيانجا - Chichewa, الآيات 8 - رقم السورة 99 - الصفحة 599.

| إِذَا زُلْزِلَتِ الْأَرْضُ زِلْزَالَهَا (1) Pamene dziko lidzagwedezeka ndi chivomerezi chomaliza | 
| وَأَخْرَجَتِ الْأَرْضُ أَثْقَالَهَا (2) Ndipo pamene nthaka idzatulutsa katundu amene ali m’kati mwake | 
| وَقَالَ الْإِنسَانُ مَا لَهَا (3) Ndipo munthu adzafunsa: “Kodi yatani?” | 
| يَوْمَئِذٍ تُحَدِّثُ أَخْبَارَهَا (4) Pa tsikuli nthaka idzaulula zonse | 
| بِأَنَّ رَبَّكَ أَوْحَىٰ لَهَا (5) Chifukwa Ambuye wako wayiuza kuti itero | 
| يَوْمَئِذٍ يَصْدُرُ النَّاسُ أَشْتَاتًا لِّيُرَوْا أَعْمَالَهُمْ (6) Pa tsikuli mtundu wa anthu udzadza m’magulu osiyana siyana kudzalangizidwa ntchito zawo | 
| فَمَن يَعْمَلْ مِثْقَالَ ذَرَّةٍ خَيْرًا يَرَهُ (7) Motero aliyense amene amachita chabwino cholemera ngati njere ya mpiru, adzachiona | 
| وَمَن يَعْمَلْ مِثْقَالَ ذَرَّةٍ شَرًّا يَرَهُ (8) Ndipo aliyense amene amachita choipa cholemera ngati njere ya mpiru, adzachiona |